By Lindelwa Topham Thole
Bukuli linamasulidwa kuchokela mu buku langa loyamba lomwe ndinalemba lotchedwa Influence of Pastor's wives. Bukuli linabwera ndi funso lodabwitsa loti "Kodi ukudziwa kuti amayi busa ambiri kumapeto kwa nyengo adzalephera kulowa ufumu wa Mulungu" Ndinadabwa kuti funsoli likubwera bwanji? Ndipo likutanthauza chani. Koma pakhalekhale ndipamene Mzimu Woyera anayamba kuvumbulutsa Mau a mubukuli. Amayi busa, akazi a atsogoleri mu mpingo ndi maudindo osiyanasiyana komanso atsogoleri achizimayi werengani Bukuli kuti muphunzire ndi kusamalira utumiki kapena ntchito yanu
Stay updated with the latest books, offers, and news. Enter your email to subscribe to our newsletter.