By Lindelwa Topham Thole
Buku ili Atumiki mu Utumiki, linamasulidwa kuchokela mu buku la chizungu lomwe ndinalemba lotchedwa ministers in the ministry. Atumiki mu Utumiki kutanthauza atsogoleri a mpingo Abusa. Atumikiwa, Abusa anayitanidwa ndi Mulungu ndi kupatsidwa ntchito ndi Mulungu kuti akayigwira momwe mmene Mulungu anayiperekela. Kodi ndi Abusa onse amene akutumikiladi moyenera? Pezani yankho mu buku ili
Stay updated with the latest books, offers, and news. Enter your email to subscribe to our newsletter.